
Sign up to save your podcasts
Or


Genesis 14:1-16 Bukuli likupitiriza kukhala ulosi komanso nzeru. Mu mavesi amenewa mulungu akutionetsera za mfumu imene ikubwera kudzera mwa Abramu. Abramu apulumutsa Loti monga mfumu ichitira ngakhale sakutionetsera Abramu ngati mfumu. Izi zikulosera za mfumu imene mulungu anayisankha kuti ipulumutse anthu ake kuchokera ku tchimo komanso imfa. Ndipo mfumuyo ndi Yesu Khristu mwana wa mulungu yemwe ndi mbewu ya Abramu.
Genesis 14:1-16 This book remains for us a prophecy and wisdom. In these verses God is showing us of a king who is coming but is a humble king and is coming to rescue his people from sin and death. And through Abram this picture is made clear as we see Abram rescuing Lot even though he is never addressed as king.
By Gospel LifeGenesis 14:1-16 Bukuli likupitiriza kukhala ulosi komanso nzeru. Mu mavesi amenewa mulungu akutionetsera za mfumu imene ikubwera kudzera mwa Abramu. Abramu apulumutsa Loti monga mfumu ichitira ngakhale sakutionetsera Abramu ngati mfumu. Izi zikulosera za mfumu imene mulungu anayisankha kuti ipulumutse anthu ake kuchokera ku tchimo komanso imfa. Ndipo mfumuyo ndi Yesu Khristu mwana wa mulungu yemwe ndi mbewu ya Abramu.
Genesis 14:1-16 This book remains for us a prophecy and wisdom. In these verses God is showing us of a king who is coming but is a humble king and is coming to rescue his people from sin and death. And through Abram this picture is made clear as we see Abram rescuing Lot even though he is never addressed as king.

12 Listeners