Chuma mzikho zadothi

Nsembe Yokwanilitsa Chilungamo cha Mulungu


Listen Later

Kuzunzika ndi Ulemerero wa Mtumiki

13Taonani, mtumiki wanga adzapambana pa ntchito yake

adzakwezedwa ndi kulemekezedwa ndipo adzalandira ulemu waukulu kwambiri.

14Anthu ambiri atamuona anadzidzimuka,

chifukwa nkhope yake inali itasakazika; sinalinso ngati ya munthu.

Ndipo thupi lake linasakazika; silinalinso ngati la munthu.

15Momwemonso anthu a mitundu yonse adzadodoma naye,

ndipo mafumu adzatseka pakamwa pawo kusowa chonena chifukwa cha iye.

Pakuti zinthu zimene iwo sanawuzidwepo, adzaziona,

ndipo zimene sanazimvepo, adzazimvetsa.

...more
View all episodesView all episodes
Download on the App Store

Chuma mzikho zadothiBy John Joseph Matandika