Chuma mzikho zadothi

Pemphero la Ambuye Gawo 2


Listen Later

9 “Chifukwa chake pempherani motere:

“ ‘Atate athu akumwamba,

dzina lanu lilemekezedwe,

10 Ufumu wanu ubwere,

chifuniro chanu chichitike

pansi pano monga kumwamba.

11 Mutipatse chakudya chathu chalero.

12 Mutikhululukire mangawa athu,

monga ifenso tawakhululukira amangawa athu.

13 Ndipo musatitengere kokatiyesa;

koma mutipulumutse kwa woyipayo.’

...more
View all episodesView all episodes
Download on the App Store

Chuma mzikho zadothiBy John Joseph Matandika