Chuma mzikho zadothi

Tipemphere Chifukwa Chiyani?


Listen Later

LUKA 11

Yesu Aphunzitsa za ku Pemphera

1Tsiku lina Yesu amapemphera pamalo ena. Atamaliza, mmodzi wa ophunzira ake anati kwa Iye, “Ambuye tiphunzitseni kupemphera, monga momwe Yohane anaphunzitsira ophunzira ake.”

2Yesu anawawuza kuti, “Pamene mukupemphera muzinena kuti:

“ ‘Atate,

dzina lanu lilemekezedwe,

ufumu wanu ubwere.

3 Mutipatse chakudya chathu chalero,

4 mutikhululukire machimo athu,

monga ifenso timakhululukira aliyense amene watilakwira.

Ndipo musalole kuti tigwe mʼmayesero.’ ”

...more
View all episodesView all episodes
Download on the App Store

Chuma mzikho zadothiBy John Joseph Matandika